Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Chotero ndikukuuzani kuti, Aliyense wovomereza+ pamaso pa anthu kuti ali kumbali yanga, Mwana wa munthunso adzavomereza pamaso pa angelo a Mulungu kuti ali kumbali yake.+

  • Aroma 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pakuti ngati ukulengeza kwa anthu ‘mawu amene ali m’kamwa mwakowo,’+ akuti Yesu ndiye Ambuye,+ ndipo mumtima mwako ukukhulupirira kuti Mulungu anamuukitsa kwa akufa,+ udzapulumuka.+

  • Chivumbulutso 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho amene wapambana pa nkhondo+ adzavekedwa malaya akunja oyera.+ Ndipo sindidzafafaniza dzina lake m’buku la moyo,+ koma ndidzavomereza dzina lake pamaso pa Atate wanga,+ ndi pamaso pa angelo ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena