Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Inunso chimodzimodzi, mukadzaona zinthu zonsezi, mudzadziwe kuti iye ali pafupi, ali pakhomo penipeni.+

  • Luka 17:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano Afarisi atamufunsa kuti ufumu wa Mulungu udzabwera liti,+ iye anawayankha kuti: “Ufumu wa Mulungu sudzabwera mwa maonekedwe ochititsa chidwi ayi.

  • Machitidwe 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tsopano atasonkhana pamodzi, anayamba kumufunsa kuti: “Ambuye, kodi mubwezeretsa ufumu+ kwa Isiraeli pa nthawi ino?”

  • 2 Atesalonika 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 kuti musafulumire kugwedezeka pa maganizo anu, kapena kutengekatengeka ndi mawu ouziridwa+ onena kuti tsiku la Yehova lafika.+ Musatero ayi, ngakhale utakhala uthenga wapakamwa,+ kapena kalata+ yooneka ngati yachokera kwa ife.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena