6 Mudzamva phokoso la nkhondo ndi mbiri za nkhondo. Izitu zisadzakuchititseni mantha. Pakuti zimenezi ziyenera kuchitika ndithu, koma mapeto adzakhala asanafikebe.+
7 Komanso, mukadzamva phokoso la nkhondo ndi mbiri za nkhondo, musadzachite mantha. Zimenezi ziyenera kuchitika ndithu, koma mapeto adzakhala asanafikebe.+