Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kuwala+ kwenikweni kumene kumaunikira+ anthu osiyanasiyana+ kunali pafupi kubwera m’dziko.

  • Yohane 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pamenepo Yesu analankhula nawonso kuti: “Ine ndine kuwala+ kwa dziko. Wonditsatira ine sadzayenda mumdima,+ koma adzakhala nako kuwala kwa moyo.”

  • Yohane 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamene ine ndili m’dziko, ndine kuwala kwa dzikoli.”+

  • Yohane 12:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Ndabwera monga kuwala m’dziko,+ kuti aliyense wokhulupirira ine asapitirize kukhala mumdima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena