Mateyu 15:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 anatenga mitanda 7 ya mkate ija ndi nsomba zija. Atayamika, anainyemanyema n’kupatsa ophunzirawo ndipo iwo anagawira khamu la anthulo.+ Maliko 8:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno anauza anthuwo kuti akhale pansi. Kenako, anatenga mitanda 7 ya mkate ija, ndi kuyamika.+ Atatero anainyemanyema n’kupatsa ophunzira ake kuti agawe, ndipo iwo anagawira khamu la anthulo.+ Yohane 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndiyeno Yesu anatenga mitanda ya mkate ija. Atayamika, anaigawira kwa anthu onse amene anakhala pansi aja. Chimodzimodzinso ndi tinsomba tija, anatigawira kwa anthuwo mmene aliyense anafunira.+ Aroma 14:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Amene amasunga tsiku amalisungira kulemekeza Yehova. Amene amadya, amadya kuti alemekeze Yehova,+ chifukwa amayamika Mulungu.+ Amene sadya, sadya pofuna kulemekeza Yehova,+ chifukwa nayenso amayamika Mulungu.+ 1 Timoteyo 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndikutero chifukwa chakuti chilichonse cholengedwa ndi Mulungu n’chabwino,+ ndipo palibe chimene chiyenera kukanidwa+ ngati chalandiridwa moyamikira,+
36 anatenga mitanda 7 ya mkate ija ndi nsomba zija. Atayamika, anainyemanyema n’kupatsa ophunzirawo ndipo iwo anagawira khamu la anthulo.+
6 Ndiyeno anauza anthuwo kuti akhale pansi. Kenako, anatenga mitanda 7 ya mkate ija, ndi kuyamika.+ Atatero anainyemanyema n’kupatsa ophunzira ake kuti agawe, ndipo iwo anagawira khamu la anthulo.+
11 Ndiyeno Yesu anatenga mitanda ya mkate ija. Atayamika, anaigawira kwa anthu onse amene anakhala pansi aja. Chimodzimodzinso ndi tinsomba tija, anatigawira kwa anthuwo mmene aliyense anafunira.+
6 Amene amasunga tsiku amalisungira kulemekeza Yehova. Amene amadya, amadya kuti alemekeze Yehova,+ chifukwa amayamika Mulungu.+ Amene sadya, sadya pofuna kulemekeza Yehova,+ chifukwa nayenso amayamika Mulungu.+
4 Ndikutero chifukwa chakuti chilichonse cholengedwa ndi Mulungu n’chabwino,+ ndipo palibe chimene chiyenera kukanidwa+ ngati chalandiridwa moyamikira,+