Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 26:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Kunena zoona, inu mfumu amene ndikulankhula nanu mwaufulu chotere, mukudziwa bwino zimenezi. Ndili wotsimikiza kuti palibe ngakhale chimodzi mwa zinthu zimenezi, chimene simunachizindikire, pakuti izi sizinachitikire mseri.+

  • Aefeso 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 kuphatikizapo ineyo. Chitani zimenezi kuti ndikatsegula pakamwa panga kuti ndilankhule, ndizitha kulankhula+ mwaufulu+ kuti ndidziwitse ena chinsinsi chopatulika cha uthenga wabwino,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena