Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Nthawi yomweyo anayamba kulalikira za Yesu m’masunagoge,+ kuti Ameneyu ndiye Mwana wa Mulungu.

  • Machitidwe 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iwo anapitiriza ulendo wawo kuchokera ku Pega ndi kukafika ku Antiokeya wa ku Pisidiya. Kumeneko analowa m’sunagoge+ tsiku la sabata ndi kukhala pansi.

  • Machitidwe 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano Paulo ndi Baranaba ali ku Ikoniyo,+ analowa m’sunagoge+ wa Ayuda. Mmenemo analankhula bwino kwambiri moti khamu lalikulu la Ayuda limodzi ndi Agiriki+ anakhala okhulupirira.

  • Machitidwe 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komabe Paulo anali kukamba nkhani m’sunagoge+ sabata lililonse, ndipo anali kukopa Ayuda ndi Agiriki.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena