Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndimamupempha kuti ngati n’kotheka mwa chifuniro+ chake, ulendo uno wokha ndibwere kwanuko.

  • 1 Akorinto 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma ndifika kwanuko posachedwapa, Yehova akalola,+ ndipo sindidzafuna kumva mawu a odzitukumulawo, koma ndidzafuna ndione mphamvu yawo.

  • Yakobo 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’malomwake, muyenera kunena kuti: “Yehova akalola,+ tikhala ndi moyo, ndi kuchita zakutizakuti.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena