20 Ngati munafa+ limodzi ndi Khristu pa mfundo zimene ndi maziko+ a moyo wa m’dzikoli,+ n’chifukwa chiyani mukupitiriza kukhala ngati kuti mudakali mbali ya dzikoli, pogonjeranso malamulo+ akuti:
24 Iye ananyamula machimo athu+ m’thupi lake pamtengo,+ kuti tilekane ndi machimo+ n’kukhala amoyo m’chilungamo. Ndipo “munachiritsidwa ndi mabala ake.”+