Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kunyada kumafikitsa munthu ku chiwonongeko,+ ndipo mtima wodzikuza umachititsa munthu kupunthwa.+

  • 1 Akorinto 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tsopano abale, zinthu zimenezi ndazinena monga zochitika kwa ine mwini ndi Apolo+ kuti inuyo mupindule, kuti muphunzire kwa ife lamulo ili lakuti: “Musapitirire zinthu zolembedwa,”+ kuti aliyense wa inu asadzitukumule+ pokonda munthu wina n’kudana ndi wina.+

  • Agalatiya 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ngati wina akudziona kuti ndi wofunika pamene si wotero,+ akudzinyenga.

  • Aefeso 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Muziyenda modzichepetsa nthawi zonse,+ mofatsa, moleza mtima,+ ndiponso mololerana m’chikondi.+

  • 1 Petulo 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chimodzimodzinso inu anyamata. Muzigonjera+ amuna achikulire. Koma nonsenu muzichitirana zinthu modzichepetsa,+ chifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza, koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena