Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 16:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Tsopano Mulungu+ angakulimbitseni mwa uthenga wabwino umene ndikulengeza ndiponso mwa uthenga wonena za Yesu Khristu umene ukulalikidwa. Uthenga wabwino umenewu ndi wogwirizana ndi zimene zaululidwa zokhudza chinsinsi chopatulika+ chimene chakhala chobisika kuyambira nthawi zakale.

  • Agalatiya 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndinapita kumeneko chifukwa ndinauzidwa m’masomphenya kuti ndipiteko.+ Ndipo ndinafotokozera+ amuna odalirika, uthenga wabwino umene ndikuulalikira kwa anthu a mitundu ina. Ndinachita zimenezo chifukwa ndinkaopa kuti mwina ndinali kuthamanga+ popanda phindu, kapena ndinali nditathamanga kale pachabe.+ Koma ndinawafotokozera zimenezi kumbali.

  • Aefeso 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 ndiponso kuti anandiululira chinsinsi chopatulika,+ monga ndalemba kale mwachidule.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena