Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 7:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mdulidwe+ sutanthauza kalikonse, ndipo kusadulidwa+ sikutanthauza kanthu, koma kusunga malamulo a Mulungu ndiko kofunika.+

  • Agalatiya 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo ngakhale Tito,+ amene ndinali naye limodzi, sanafunikire kudulidwa,+ ngakhale kuti iye ndi Mgiriki.

  • Agalatiya 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pakuti kudulidwa kapena kusadulidwa si kanthu,+ koma chofunika ndi kukhala wolengedwa mwatsopano.+

  • Akolose 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mukatero, sipadzakhala Mgiriki kapena Myuda, kudulidwa kapena kusadulidwa, mlendo, Msukuti, kapolo, kapena mfulu,+ koma Khristu ndiye zinthu zonse ndipo ali mwa onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena