Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 25:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Nkhani yabwino yochokera kudziko lakutali+ ili ngati madzi ozizira kwa munthu wotopa.+

  • 2 Akorinto 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma osati chabe chifukwa tinali ndi Tito, komanso chifukwa cha mmene inuyo munamulimbikitsira, pamene anatibweretsera uthenga+ wakuti mukufunitsitsa kulapa, muli ndi chisoni, ndiponso mukundidera nkhawa. Nditamva zimenezi ndinakondweranso kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena