Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 16:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho anamuitana ndi kumuuza kuti, ‘Ndamva zoipa zimene ukuchita. Pita ukalembe lipoti la mmene wagwirira ntchito yoyang’anira nyumba ino udzandipatse,+ pakuti supitiriza kuyendetsa ntchito za panyumba pano.’

  • 1 Akorinto 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndikachita zimenezi mwaufulu,+ ndili ndi mphoto.+ Koma ndikachita motsutsana ndi kufuna kwanga, sindingachitire mwina, ndinebe woyang’anira mogwirizana ndi udindo+ umene unaikidwa m’manja mwanga.

  • Aefeso 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndithudi munamva kuti ndinaikidwa kukhala woyang’anira+ kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu kuti ndikuthandizeni,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena