Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 3:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndiponso, kuyesedwa olungama chifukwa cha kukoma mtima kwake kwakukulu+ kumene wakusonyeza, powamasula ndi dipo+ lolipiridwa ndi Khristu Yesu, kuli ngati mphatso yaulere.+

  • Agalatiya 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Popeza tikudziwa kuti munthu amayesedwa wolungama+ mwa kukhulupirira+ Khristu Yesu, osati chifukwa cha ntchito za chilamulo, ife takhulupirira Khristu Yesu. Tachita zimenezi kuti tiyesedwe olungama chifukwa cha chikhulupiriro chathu mwa Khristu,+ osati mwa ntchito zotsatira chilamulo. Tatero chifukwa palibe munthu adzayesedwa wolungama chifukwa cha ntchito zotsatira chilamulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena