Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 8:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiponso, amene anawasankhiratu+ ndi amenenso anawaitana,+ ndipo amene anawaitanawo ndi amenenso anawayesa olungama.+ Kenako amene anawayesa olungama ndi amenenso anawapatsa ulemerero.+

  • 1 Akorinto 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mulungu amene anakuitanani kuti mukhale oyanjana+ ndi Mwana wake Yesu Khristu, Ambuye wathu, ndi wokhulupirika.+

  • Afilipi 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndikuyesetsa kuchita zimenezi mpaka nditapeza+ mphoto+ ya chiitano cha Mulungu chopita kumwamba,+ chodzera mwa Khristu Yesu.

  • 1 Atesalonika 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 n’cholinga choti mupitirize kuyenda+ m’njira imene Mulungu, amene akukuitanani+ ku ufumu+ wake ndi ulemerero, amafuna.

  • 2 Timoteyo 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iye anatipulumutsa+ ndi kutiitana kuti tikhale oyera,+ osati chifukwa cha ntchito zathu,+ koma mwa chifuniro chake ndi kukoma mtima kwake kwakukulu. Iye anatikomera mtima m’njira imeneyi kalekalelo mwa Khristu Yesu.+

  • 2 Petulo 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa chifukwa chimenechi abale, chitani chilichonse chotheka kuti mukhalebe okhulupirika, n’cholinga choti mupitirizebe kukhala pakati pa anthu amene Mulungu wawaitana+ ndi kuwasankha,+ pakuti mukapitiriza kuchita zinthu zimenezi simudzalephera ngakhale pang’ono.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena