Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Yohane 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Aliyense amene ali wogwirizana+ ndi Yesu sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo.+ Aliyense amene amachita tchimo ndiye kuti sanamuone kapena kumudziwa.+

  • 1 Yohane 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aliyense amene ali mwana wa Mulungu sapitiriza kuchita tchimo,+ chifukwa mbewu ya Mulungu yopatsa moyo imakhalabe mwa munthu ameneyo, ndipo sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo, chifukwa ndi mwana wa Mulungu.+

  • 1 Yohane 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ife tikudziwa ndipo tikukhulupirira za chikondi+ chimene Mulungu ali nacho kwa ife.

      Mulungu ndiye chikondi,+ ndipo munthu amene amapitiriza kusonyeza chikondi,+ amakhalabe wogwirizana ndi Mulungu ndiponso Mulungu amakhala wogwirizana+ naye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena