Ekisodo 33:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndipo anawonjezera kuti: “Sungathe kuona nkhope yanga, chifukwa palibe munthu angandione n’kukhalabe ndi moyo.”+ Yohane 1:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Palibe munthu anaonapo Mulungu ndi kale lonse,+ mulungu wobadwa yekha+ amene ali pachifuwa+ cha Atate ndiye amene anafotokoza za Mulungu.+ Yohane 4:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Mulungu ndiye Mzimu,+ ndipo onse omulambira ayenera kumulambira motsogoleredwa ndi mzimu ndi choonadi.”+ Yohane 5:37 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 37 Komanso Atate amene anandituma andichitira umboni.+ Inu simunamvepo mawu ake nthawi ina iliyonse, kapena kuona thupi lake.+ Yohane 6:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Sikuti alipo munthu amene anaonapo Atate ayi,+ kupatulapo yekhayo amene anachokera kwa Mulungu, ameneyu anaona Atate.+
20 Ndipo anawonjezera kuti: “Sungathe kuona nkhope yanga, chifukwa palibe munthu angandione n’kukhalabe ndi moyo.”+
18 Palibe munthu anaonapo Mulungu ndi kale lonse,+ mulungu wobadwa yekha+ amene ali pachifuwa+ cha Atate ndiye amene anafotokoza za Mulungu.+
24 Mulungu ndiye Mzimu,+ ndipo onse omulambira ayenera kumulambira motsogoleredwa ndi mzimu ndi choonadi.”+
37 Komanso Atate amene anandituma andichitira umboni.+ Inu simunamvepo mawu ake nthawi ina iliyonse, kapena kuona thupi lake.+
46 Sikuti alipo munthu amene anaonapo Atate ayi,+ kupatulapo yekhayo amene anachokera kwa Mulungu, ameneyu anaona Atate.+