-
Ezekieli 47:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 “M’mbali mwa mtsinjewo mudzamera mitengo yosiyanasiyana ya zipatso. Mitengoyo idzamera m’mphepete mwenimweni kumbali iyi ndi mbali inayo.+ Masamba ake sadzafota+ ndipo zipatso zake sizidzatha.+ Mitengo imeneyo izidzabereka zipatso mwezi ndi mwezi chifukwa chakuti madzi ake akuchokera m’malo opatulika.+ Zipatso zake zidzakhala chakudya ndipo masamba ake adzakhala mankhwala.”+
-