Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 2
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 2:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 14:25; De 1:40

Deuteronomo 2:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:7

Deuteronomo 2:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 36:8; Nu 20:14; De 23:7
  • +Ge 27:40; 36:10
  • +Ge 27:39; 36:9; De 2:8
  • +Eks 15:15; 23:27; De 2:25

Deuteronomo 2:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 32:3; 36:8; De 32:8; Yos 24:4; 2Mb 20:10; Mac 17:26

Deuteronomo 2:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:19

Deuteronomo 2:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 12:2; Miy 10:22
  • +De 8:2; 29:5; Sl 95:10; Mac 13:18
  • +Ne 9:21; Sl 23:1; 34:9, 10; 37:25; Afi 4:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    1/2022, ptsa. 5-6

Deuteronomo 2:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:20, 21; 21:4; Owe 11:18
  • +De 11:30
  • +2Mb 8:17
  • +Nu 21:13; Owe 11:17; 2Mb 20:10

Deuteronomo 2:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:15; De 2:18; Yes 15:1
  • +Ge 19:37

Deuteronomo 2:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 14:5
  • +Nu 13:33; Yos 14:15

Deuteronomo 2:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 14:5; De 3:11; 1Mb 20:6
  • +Nu 13:22, 28, 33; De 1:28; 9:2

Deuteronomo 2:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 14:6; 36:20; 1Mb 1:39
  • +Ge 36:10
  • +Ge 27:39, 40

Deuteronomo 2:13

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Ge 26:17.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:12

Deuteronomo 2:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 14:33; 32:11; De 1:35; Sl 95:11; 106:26; Eze 20:15; Ahe 3:18; Yuda 5

Deuteronomo 2:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ahe 10:31
  • +1Ak 10:5

Deuteronomo 2:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 26:64

Deuteronomo 2:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:15, 28

Deuteronomo 2:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 19:38; De 2:9; Owe 11:15; 2Mb 20:10; Mac 17:26

Deuteronomo 2:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 15:20; De 3:11; Yos 17:15

Deuteronomo 2:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:33; De 2:10; 9:2
  • +Eks 15:3; Sl 24:8

Deuteronomo 2:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 36:8
  • +Ge 14:6; 36:20; De 2:12

Deuteronomo 2:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 13:3
  • +Ge 10:19; Yos 11:22
  • +Ge 10:14; 1Mb 1:12
  • +Yer 47:4; Amo 9:7; Mac 27:13

Deuteronomo 2:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:13; Owe 11:18
  • +Nu 21:23; Yos 9:10

Deuteronomo 2:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:14; 23:27; De 11:25; Yos 2:9

Deuteronomo 2:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 20:10
  • +Yos 13:18; 21:37
  • +Nu 21:21

Deuteronomo 2:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:22; Owe 11:19

Deuteronomo 2:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:19

Deuteronomo 2:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:8
  • +De 2:9, 18
  • +De 9:5; Yos 1:11

Deuteronomo 2:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yob 34:11; Aro 9:18
  • +Nu 21:25; Sl 135:10; 136:18

Deuteronomo 2:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 32:33; Sl 135:12

Deuteronomo 2:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:23; Owe 11:20

Deuteronomo 2:33

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 20:13; Ne 9:22; Sl 135:11; 136:18
  • +Nu 21:24; De 29:7

Deuteronomo 2:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 27:28; Nu 31:17; De 20:16, 17

Deuteronomo 2:35

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 8:27

Deuteronomo 2:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 3:12; 4:48; Yos 13:9
  • +Yos 1:5; Sl 44:3

Deuteronomo 2:37

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 3:16; Owe 11:15
  • +Nu 21:24; Yos 12:2

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 2:1Nu 14:25; De 1:40
Deut. 2:3De 2:7
Deut. 2:4Ge 36:8; Nu 20:14; De 23:7
Deut. 2:4Ge 27:40; 36:10
Deut. 2:4Ge 27:39; 36:9; De 2:8
Deut. 2:4Eks 15:15; 23:27; De 2:25
Deut. 2:5Ge 32:3; 36:8; De 32:8; Yos 24:4; 2Mb 20:10; Mac 17:26
Deut. 2:6Nu 20:19
Deut. 2:7De 8:2; 29:5; Sl 95:10; Mac 13:18
Deut. 2:7Ne 9:21; Sl 23:1; 34:9, 10; 37:25; Afi 4:19
Deut. 2:7Ge 12:2; Miy 10:22
Deut. 2:8Nu 20:20, 21; 21:4; Owe 11:18
Deut. 2:8De 11:30
Deut. 2:82Mb 8:17
Deut. 2:8Nu 21:13; Owe 11:17; 2Mb 20:10
Deut. 2:9Nu 21:15; De 2:18; Yes 15:1
Deut. 2:9Ge 19:37
Deut. 2:10Ge 14:5
Deut. 2:10Nu 13:33; Yos 14:15
Deut. 2:11Ge 14:5; De 3:11; 1Mb 20:6
Deut. 2:11Nu 13:22, 28, 33; De 1:28; 9:2
Deut. 2:12Ge 14:6; 36:20; 1Mb 1:39
Deut. 2:12Ge 36:10
Deut. 2:12Ge 27:39, 40
Deut. 2:13Nu 21:12
Deut. 2:14Nu 14:33; 32:11; De 1:35; Sl 95:11; 106:26; Eze 20:15; Ahe 3:18; Yuda 5
Deut. 2:15Ahe 10:31
Deut. 2:151Ak 10:5
Deut. 2:16Nu 26:64
Deut. 2:18Nu 21:15, 28
Deut. 2:19Ge 19:38; De 2:9; Owe 11:15; 2Mb 20:10; Mac 17:26
Deut. 2:20Ge 15:20; De 3:11; Yos 17:15
Deut. 2:21Nu 13:33; De 2:10; 9:2
Deut. 2:21Eks 15:3; Sl 24:8
Deut. 2:22Ge 36:8
Deut. 2:22Ge 14:6; 36:20; De 2:12
Deut. 2:23Yos 13:3
Deut. 2:23Ge 10:19; Yos 11:22
Deut. 2:23Ge 10:14; 1Mb 1:12
Deut. 2:23Yer 47:4; Amo 9:7; Mac 27:13
Deut. 2:24Nu 21:13; Owe 11:18
Deut. 2:24Nu 21:23; Yos 9:10
Deut. 2:25Eks 15:14; 23:27; De 11:25; Yos 2:9
Deut. 2:26De 20:10
Deut. 2:26Yos 13:18; 21:37
Deut. 2:26Nu 21:21
Deut. 2:27Nu 21:22; Owe 11:19
Deut. 2:28Nu 20:19
Deut. 2:29De 2:8
Deut. 2:29De 2:9, 18
Deut. 2:29De 9:5; Yos 1:11
Deut. 2:30Yob 34:11; Aro 9:18
Deut. 2:30Nu 21:25; Sl 135:10; 136:18
Deut. 2:31Nu 32:33; Sl 135:12
Deut. 2:32Nu 21:23; Owe 11:20
Deut. 2:33De 20:13; Ne 9:22; Sl 135:11; 136:18
Deut. 2:33Nu 21:24; De 29:7
Deut. 2:34Le 27:28; Nu 31:17; De 20:16, 17
Deut. 2:35Yos 8:27
Deut. 2:36De 3:12; 4:48; Yos 13:9
Deut. 2:36Yos 1:5; Sl 44:3
Deut. 2:37De 3:16; Owe 11:15
Deut. 2:37Nu 21:24; Yos 12:2
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 2:1-37

Deuteronomo

2 “Ndiyeno tinatembenuka ndi kulowera kuchipululu kudzera njira ya ku Nyanja Yofiira, monga mmene Yehova anandiuzira.+ Ndipo tinayenda masiku ambiri m’dera lapafupi ndi phiri la Seiri. 2 Kenako Yehova anandiuza kuti, 3 ‘Mwayenda kwa nthawi yaitali m’dera lapafupi ndi phirili.+ Tembenukani ndi kulowera kumpoto. 4 Auze anthuwo kuti: “Mukudutsa m’malire a dziko la abale anu,+ ana a Esau,+ amene akukhala m’Seiri.+ Iwo adzachita nanu mantha,+ choncho muyenera kukhala osamala kwambiri. 5 Musalimbane nawo, chifukwa sindikupatsani dziko lawo, ngakhale kachigawo kokwana phazi limodzi lokha. Ndinapereka phiri la Seiri kwa Esau kuti likhale malo ake.+ 6 Mudzadya chakudya chimene mudzagula kwa iwo ndi ndalama, ndipo mudzamwa madzi amene mudzagula kwa iwo ndi ndalama.+ 7 Yehova Mulungu wanu wakudalitsani pa chilichonse chimene dzanja lanu likuchita.+ Iye akudziwa za kuyenda kwanu kudutsa m’chipululu chachikulu ichi. Yehova Mulungu wanu wakhala nanu zaka 40 zimenezi,+ ndipo simunasowe kanthu.”’+ 8 Chotero tinalambalala abale athu, ana a Esau,+ amene akukhala m’Seiri, ndipo sitinayende njira ya Araba,+ Elati ndi Ezioni-geberi.+

“Kenako tinatembenuka ndi kudutsa njira ya m’chipululu cha Mowabu.+ 9 Pamenepo Yehova anandiuza kuti, ‘Usavutitse Amowabu kapena kuchita nawo nkhondo, chifukwa sindidzakupatsa mbali iliyonse ya dziko lawo kuti likhale lako. Ndinapereka Ari+ kwa ana a Loti kuti akhale malo awo.+ 10 (Kale munali kukhala Aemi,+ anthu amphamvu kwambiri ndiponso ochuluka. Iwo anali ataliatali ngati Aanaki.+ 11 Arefai+ anali kuonedwanso ngati Aanaki,+ ndipo Amowabu anali kutcha Arefaiwo kuti Aemi. 12 Kale Ahori+ anali kukhala m’Seiri, ndipo ana a Esau+ anawalanda dzikolo ndi kuwapha. Atatero, ana a Esauwo anayamba kukhala m’dzikolo,+ monga mmene ana a Isiraeli ayenera kuchitira m’dziko lawo, limene Yehova adzawapatsa ndithu.) 13 Choncho nyamukani ndi kudutsa chigwa* cha Zeredi.’ Pamenepo tinadutsadi chigwa cha Zeredi.+ 14 Ndipo masiku amene tinayenda kuchokera ku Kadesi-barinea mpaka kuwoloka chigwa cha Zeredi anali zaka 38, kufikira m’badwo wa amuna otha kupita kunkhondo utatha pakati panu, monga mmene Yehova analumbirira kwa iwo.+ 15 Dzanja+ la Yehova linali pa iwo kuwasautsa ndi kuwachotsa pakati panu, kufikira onse atatha.+

16 “Ndiyeno amuna onse otha kupita kunkhondo atatha kufa pakati pa anthu,+ 17 Yehova analankhulanso ndi ine, kuti, 18 ‘Lero udutsa m’dera la Mowabu, pafupi ndi Ari,+ 19 ndipo uyandikire pafupi ndi ana a Amoni. Usawavutitse kapena kumenyana nawo, chifukwa sindidzakupatsa mbali iliyonse ya dziko la ana a Amoni kuti likhale lako. Dziko limeneli ndinalipereka kwa ana a Loti kuti likhale lawo.+ 20 Dzikoli linali kudziwika kuti ndi la Arefai.+ (Kale munali kukhala Arefai ndipo Aamoni anali kutcha Arefaiwo kuti Azamuzumi. 21 Anthu amenewa anali amphamvu kwambiri ndiponso ochuluka. Analinso ataliatali ngati Aanaki.+ Yehova anawafafaniza+ kuwachotsa pamaso pa ana a Amoni kuti ana a Amoniwo atenge dzikolo ndi kukhalamo, 22 monga mmene anachitira ndi ana a Esau amene akukhala m’Seiri.+ Iye anafafaniza Ahori+ kuwachotsa pamaso pa ana a Esau, kuti ana a Esauwo atenge dzikolo ndi kukhalamo mpaka lero. 23 Aavi+ amene anali kukhala m’midzi mpaka kukafika ku Gaza,+ anawonongedwa ndi Akafitori+ ochokera ku Kafitori,+ kuwachotsa pamaso pawo kuti Akafitoriwo akhale m’dzikolo.)

24 “‘Nyamukani, muyende ndi kudutsa chigwa cha Arinoni.+ Taonani, ndapereka m’manja mwanu Sihoni,+ Mwamori, mfumu ya Hesiboni. Yambani kulanda dziko lake, ndipo menyanani naye nkhondo. 25 Lero ndichititsa anthu a mitundu ina okhala pansi pa thambo, amene adzamva za inu, kuchita nanu mantha kwambiri ndi kuyamba kukuopani. Chifukwa cha inu, iwo adzanthunthumira ndi kumva zopweteka zofanana ndi zowawa za pobereka.’+

26 “Kenako, ndinatumiza amithenga a mawu amtendere+ kuchokera m’chipululu cha Kademoti,+ kupita kwa Sihoni+ mfumu ya Hesiboni, kuti, 27 ‘Ndilole ndidutse m’dziko lako. Ndidzangodutsa mumsewu. Sindidzatembenukira kudzanja lamanja kapena lamanzere.+ 28 Ndidzadya chakudya chimene udzandigulitsa ndi ndalama, ndipo ndidzamwa madzi amene udzandigulitsa ndi ndalama. Ndilole ndingodutsa m’dziko lako,+ 29 monga mmene ana a Esau amene akukhala m’Seiri+ ndi Amowabu+ amene akukhala mu Ari anachitira kwa ine. Ndidzadutsa m’dziko lako mpaka kukawoloka Yorodano, kulowa m’dziko limene Yehova Mulungu wathu anatipatsa.’+ 30 Koma Sihoni mfumu ya Hesiboni sanatilole kudutsa m’dziko lake, chifukwa Yehova Mulungu wanu anamulola kuti akhale wokanika+ ndi kuti aumitse mtima wake. Anatero kuti am’pereke m’manja mwanu monga mmene zilili lero.+

31 “Zitatero, Yehova anandiuza kuti, ‘Taona, ndikupereka Sihoni ndi dziko lake kwa iwe. Yamba kulanda dziko lake.’+ 32 Sihoni atatuluka pamodzi ndi anthu ake onse kudzamenyana nafe nkhondo ku Yahazi,+ 33 Yehova Mulungu wathu anam’pereka kwa ife,+ ndipo tinam’gonjetsa+ limodzi ndi ana ake ndi anthu ake onse. 34 Tinalandanso mizinda yake yonse pa nthawi imeneyo ndi kuwononga mzinda wina uliwonse.+ Tinapha amuna, akazi ndi ana, ndipo sitinasiye munthu aliyense wamoyo. 35 Ziweto zokha n’zimene tinatenga monga zofunkha pamodzi ndi zofunkha za m’mizinda imene tinalanda.+ 36 Kuchokera ku Aroweli,+ mzinda umene uli m’mbali mwa chigwa cha Arinoni, ndiponso kuchokera kumzinda wa m’chigwa mpaka ku Giliyadi, panalibe mzinda womwe unali wa malinga aatali kwambiri kwa ife.+ Yehova Mulungu wathu anawapereka onsewo kwa ife. 37 Koma simunayandikire dziko la ana a Amoni,+ dera lonse la m’mbali mwa chigwa cha Yaboki,+ kapena mizinda ya m’dera lamapiri, kapenanso malo alionse amene Yehova Mulungu wathu sanatilamule kuti tiwalande.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena