Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yosefe+ ndi mphukira yamtengo wobala zipatso. Iye ndi mtengo wobala zipatso pakasupe, umene nthambi zake zimafika pamwamba pa khoma la mpanda.

  • Genesis 49:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Iye* ndi wochokera kwa Mulungu wa bambo ako ndipo adzakuthandiza. Iye ali ndi Wamphamvuyonse, ndipo Mulunguyo adzakudalitsa pokupatsa madzi ochokera kumwamba ndi pansi pa nthaka.+ Adzakudalitsa pokupatsa ana ndi ziweto zambiri.*

  • Machitidwe 7:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mitu ya mabanjayo inachitira nsanje Yosefe+ nʼkumugulitsa ku Iguputo.+ Koma Mulungu anali naye,+ 10 ndipo anamupulumutsa mʼmavuto ake onse. Komanso ankamukonda ndipo ankamuthandiza kuti azichita zinthu mwanzeru pamaso pa Farao mfumu ya Iguputo. Faraoyo anapatsa Yosefe udindo woti aziyangʼanira Iguputo ndi nyumba yake yonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena