Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 26:44, 45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Ana aamuna a Aseri+ potengera mabanja awo anali awa: Imuna amene anali kholo la banja la Aimuna, Isivi amene anali kholo la banja la Aisivi ndi Beriya amene anali kholo la banja la Aberiya. 45 Ana aamuna a Beriya anali Hiberi amene anali kholo la banja la Ahiberi ndi Malikieli amene anali kholo la banja la Amalikieli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena