Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho Yehova anati: “Ndidzaseseratu padziko lapansi anthu amene ndinawalenga. Ndidzaseseratu anthu, nyama zoweta, nyama zokwawa komanso zamoyo zouluka mumlengalenga, chifukwa ndikumva chisoni kuti ndinazipanga.”

  • 2 Petulo 3:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anthu amenewa amanyalanyaza mwadala mfundo yakuti, kalero panali kumwamba ndi dziko lapansi lomwe linatuluka mʼmadzi ndi kuima pamwamba pa madziwo chifukwa cha mawu a Mulungu.+ 6 Ndipo kudzera mʼzinthu zimenezi, dziko la pa nthawiyo linawonongedwa pamene linamira mʼmadzi a chigumula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena