Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Mulungu anati: “Kumwamba kukhale zounikira+ kuti zilekanitse masana ndi usiku+ ndipo zidzakhala zizindikiro zosonyeza nyengo, masiku ndi zaka.+

  • Salimo 74:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Munaika malire onse a dziko lapansi.+

      Munapanga nyengo yachilimwe ndi nyengo yachisanu.+

  • Mlaliki 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mʼbadwo umapita ndipo mʼbadwo wina umabwera,

      Koma dziko lapansi lidzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena