Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Mulungu anauza Abulahamu kuti: “Mkazi wako Sarai,*+ usamamuitanenso kuti Sarai, chifukwa dzina lake tsopano likhala Sara.* 16 Ndidzamudalitsa ndipo adzakuberekera mwana wamwamuna.+ Iye ndidzamudalitsa moti adzakhala mayi wa mitundu yambiri ya anthu ndi wa mafumu a mitundu yambiri ya anthu.”

  • Genesis 21:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kenako Mulungu anauza Abulahamu kuti: “Usaipidwe ndi zimene Sara akukuuza zokhudza mnyamatayo ndiponso kapolo wakoyo. Mumvere,* chifukwa mbadwa* zimene ndinakulonjeza zidzachokera mwa Isaki.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena