Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndi ndani anatseka nyanja ndi zitseko,+

      Pamene inaphulika kuchokera mʼmimba,

  • Yobu 38:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiye ndinati, ‘Ukhoza kufika apa, koma usapitirirepo,

      Ndipo mafunde ako aatali azilekezera pamenepaʼ?+

  • Salimo 104:6-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Munaliphimba ndi madzi ozama ngati kuti mwaliphimba ndi nsalu.+

      Madziwo anakwera kupitirira mapiri.

       7 Chifukwa cha kudzudzula kwanu, madziwo anathawa.+

      Atamva mabingu anu anayamba kuthawa mopanikizika kwambiri

       8 Kupita kumalo amene munawakonzera.

      Mapiri anakwera+ ndipo zigwa zinatsika.

       9 Munawaikira malire kuti asapitirire malirewo,+

      Kuti asadzamizenso dziko lapansi.

  • Salimo 136:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,+

      Chifukwa chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena