Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 2:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo anawauza kuti: “Ndikudziwa kuti Yehova akupatsani dzikoli+ ndipo tonse tikuchita nanu mantha.+ Aliyense mʼdzikoli mtima wake suli mʼmalo chifukwa cha inu.+ 10 Tinamva mmene Yehova anaphwetsera madzi a Nyanja Yofiira pamene munkachoka ku Iguputo.+ Komanso mmene munaphera mafumu awiri a Aamori, Sihoni+ ndi Ogi,+ kutsidya* kwa mtsinje wa Yorodano.

  • Salimo 66:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anasandutsa nyanja kukhala malo ouma,+

      Anthu anawoloka mtsinje poyenda ndi mapazi awo.+

      Pamenepo tinasangalala chifukwa cha zimene Mulungu anatichitira.+

  • Salimo 106:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye analamula* ndipo Nyanja Yofiira inauma.

      Anatsogolera anthu ake kudutsa pakati pa madzi akuya ngati akudutsa mʼchipululu.+

  • Salimo 114:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Nyanja inaona zimenezi ndipo inathawa,+

      Yorodano anabwerera mʼmbuyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena