Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako mfumu ya Iguputo inauzidwa kuti Aisiraeli athawa. Nthawi yomweyo mtima wa Farao ndi atumiki ake unasinthanso ataganizira za Aisiraeli,+ moti anati: “Nʼchifukwa chiyani tachita zimenezi? Nʼchifukwa chiyani talola kuti akapolo athu Aisiraeli achoke?”

  • Ekisodo 14:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aiguputo ankawathamangira,+ ndipo magaleta onse a Farao, asilikali apamahatchi ndi gulu lake lankhondo anawayandikira. Aisiraeliwo anali atamanga msasa mʼmphepete mwa nyanja, pafupi ndi Pihahiroti moyangʼanizana ndi Baala-zefoni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena