Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsopano mukadzamvera mawu anga mosamala ndi kusunga pangano langa, mudzakhaladi chuma changa chapadera pa anthu onse,+ chifukwa dziko lonse lapansi ndi langa.+

  • Ekisodo 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ngati simupita nafe, kodi anthu adziwa bwanji kuti ine ndi anthu anuwa mwatikomera mtima? Koma mukapita nafe+ zisonyeza kuti ine ndi anthu anuwa mwatisiyanitsa ndi anthu ena onse amene ali padziko lapansi.”+

  • 1 Mafumu 8:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Chifukwa munawasankha pakati pa mitundu yonse ya anthu apadziko lapansi+ kuti akhale cholowa chanu ngati mmene munanenera kudzera mwa Mose mtumiki wanu, pamene munkatulutsa makolo athu mu Iguputo, inu Yehova Ambuye Wamkulu Koposa.”

  • 1 Petulo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma inu ndi “fuko losankhidwa mwapadera, ansembe achifumu, mtundu woyera+ ndiponso anthu oti adzakhale chuma chapadera.+ Mwasankhidwa kuti mulengeze makhalidwe abwino kwambiri”+ a Mulungu amene anakuitanani kuti muchoke mumdima ndipo anakulandirani mʼkuwala kwake kodabwitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena