Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Kachitsuloko kazikhala pamphumi pa Aroni. Munthu akachimwira zinthu zopatulika+ zimene Aisiraeli amaziyeretsa akamazipereka ngati mphatso zopatulika, Aroni aziyankha mlandu wa tchimo limenelo. Kachitsuloko kazikhala pamphumi pake nthawi zonse, kuti azichititsa anthuwo kukhala ovomerezeka pamaso pa Yehova.

  • Numeri 18:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Mukapereka zinthu zabwino koposa kuchokera pa zinthu zimenezi, simudzachimwa ngati mutadya, komanso musaipitse zinthu zopatulika za Aisiraeli, kuti musafe.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena