Deuteronomo 30:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Yehova Mulungu wanu adzayeretsa* mitima yanu ndi mitima ya ana anu,+ kuti muzikonda Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse komanso moyo wanu wonse ndipo mudzakhala ndi moyo.+ Yeremiya 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Chitani mdulidwe pamaso pa Yehova,Chitani mdulidwe wa mitima yanu,+Inu anthu a ku Yuda komanso anthu amene mukukhala mu Yerusalemu,Kuti mkwiyo wanga usayake ngati moto,Usayake popanda aliyense wowuzimitsa,Chifukwa cha zochita zanu zoipa.”+ Machitidwe 7:51 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 51 Anthu okanika inu ndiponso osachita mdulidwe wamumtima ndi mʼmakutu. Nthawi zonse mumatsutsana ndi mzimu woyera. Mukuchita zinthu ngati mmene ankachitira makolo anu.+
6 Yehova Mulungu wanu adzayeretsa* mitima yanu ndi mitima ya ana anu,+ kuti muzikonda Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse komanso moyo wanu wonse ndipo mudzakhala ndi moyo.+
4 Chitani mdulidwe pamaso pa Yehova,Chitani mdulidwe wa mitima yanu,+Inu anthu a ku Yuda komanso anthu amene mukukhala mu Yerusalemu,Kuti mkwiyo wanga usayake ngati moto,Usayake popanda aliyense wowuzimitsa,Chifukwa cha zochita zanu zoipa.”+
51 Anthu okanika inu ndiponso osachita mdulidwe wamumtima ndi mʼmakutu. Nthawi zonse mumatsutsana ndi mzimu woyera. Mukuchita zinthu ngati mmene ankachitira makolo anu.+