Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mulungu anamva pemphero la Leya ndipo anakhala woyembekezera. Patapita nthawi, Leya anaberekera Yakobo mwana wamwamuna wa 5. 18 Mwanayo atabadwa, Leya anati: “Mulungu wandipatsa mphoto* chifukwa ndapereka kapolo wanga kwa mwamuna wanga.” Choncho Leya anapatsa mwanayo dzina lakuti Isakara.*+

  • Genesis 46:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana a Isakara anali Tola, Puva, Yabi ndi Simironi.+

  • Numeri 2:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pafupi ndi fuko limeneli kuzikhala fuko la Isakara. Mtsogoleri wa ana a Isakara ndi Netaneli,+ mwana wa Zuwara. 6 Asilikali ake amene analembedwa mayina alipo 54,400.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena