Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 43:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Yosefe atakweza maso ake nʼkuona mngʼono wake Benjamini, mʼbale wake wa mimba imodzi,+ anati: “Kodi uyu ndi mngʼono wanu amene munkanena uja?”+ Ananenanso kuti: “Mulungu akukomere mtima mwana wanga.”

  • Genesis 46:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ana a Benjamini+ anali Bela, Bekeri, Asibeli, Gera,+ Namani, Ehi, Rosi, Mupimu, Hupimu+ ndi Aridi.+

  • Numeri 2:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kenako pazibwera fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa ana a Benjamini ndi Abidana,+ mwana wa Gidiyoni. 23 Asilikali ake amene analembedwa mayina alipo 35,400.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena