Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno mngelo wa Mulungu woona+ amene ankayenda patsogolo pa Aisiraeli anachoka nʼkupita kumbuyo kwawo. Ndipo chipilala cha mtambo chija chinachoka kutsogolo nʼkukaima kumbuyo kwawo.+

  • Ekisodo 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndikukutumizirani mngelo patsogolo panu+ kuti azikutetezani mʼnjira komanso kukakulowetsani mʼdziko limene ndakukonzerani.+

  • Ekisodo 33:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndidzatumiza mngelo patsogolo panu+ ndipo ndidzathamangitsa Akanani, Aamori, Ahiti, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena