-
Genesis 12:2, 3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndidzakupangitsa kuti ukhale mtundu waukulu. Ndidzakudalitsa ndipo ndidzapangitsa kuti dzina lako litchuke. Komanso anthu ena adzadalitsidwa chifukwa cha iwe.+ 3 Odalitsa iwe ndidzawadalitsa, ndipo wotemberera iwe ndidzamutemberera.+ Mabanja onse apadziko lapansi adzadalitsidwa* kudzera mwa iwe.”+
-
-
Maliro 3:64Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
64 Inu Yehova, mudzawabwezera mogwirizana ndi zochita zawo.
-