Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Njira ya Mulungu woona ndi yangwiro.+

      Mawu a Yehova ndi oyengeka bwino.+

      Iye ndi chishango kwa onse othawira kwa iye.+

  • Salimo 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova ndi thanthwe langa, malo anga achitetezo ndiponso amene amandipulumutsa.+

      Mulungu wanga ndi thanthwe langa+ limene ndimathawirako,

      Iye ndi chishango changa, nyanga* yanga ya chipulumutso* komanso malo anga othawirako otetezeka.*+

  • Salimo 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa mphamvu.*+

      Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+

  • Yakobo 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwiro imachokera kumwamba.+ Imatsika kuchokera kwa Atate wa zounikira zakuthambo,+ amene sasintha ngati mthunzi umene umasunthasuntha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena