Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Yehova Mulungu wanu akadzakulowetsani mʼdziko limene mwatsala pangʼono kulitenga kuti likhale lanu,+ adzakuchotseraninso mitundu ikuluikulu.+ Adzakuchotserani Ahiti, Agirigasi, Aamori,+ Akanani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi,+ mitundu 7 ikuluikulu komanso yamphamvu kuposa inu.+ 2 Yehova Mulungu wanu adzawapereka kwa inu ndipo mudzawagonjetsa.+ Mudzawawononge+ ndithu ndipo musadzachite nawo pangano lililonse kapena kuwakomera mtima.+

  • Deuteronomo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma mʼmizinda ya anthu awa, imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, musalole kuti mutsale chamoyo chilichonse.+

  • Yoswa 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsiku limenelo, Yoswa analanda mzinda wa Makeda+ ndipo anapha anthu amumzindawo ndi lupanga. Anapha mfumu ya mzindawo ndi anthu ake onse, ndipo anaonetsetsa kuti pasakhale wopulumuka.+ Mfumu ya ku Makeda+ anaichita zofanana ndi zomwe anaichita mfumu ya ku Yeriko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena