Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kanani anabereka Sidoni,+ mwana wake woyamba, kenako anabereka Heti.+

  • Genesis 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ahivi,+ Aariki, Asini,

  • Genesis 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Sekemu mwana wamwamuna wa Hamori Mhivi,+ mmodzi wa atsogoleri amumzindawu ataona mtsikanayu, anamutenga nʼkumugwiririra.

  • Ekisodo 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho ndipita kuti ndikawapulumutse mʼmanja mwa Aiguputo+ ndi kuwatulutsa mʼdzikolo nʼkuwalowetsa mʼdziko labwino komanso lalikulu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ndiwalowetsa mʼdziko la Akanani, Ahiti, Aamori, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena