Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 14:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho Samisoni anapita ku Timuna pamodzi ndi bambo ndi mayi ake. Atafika mʼminda ya mpesa ya ku Timuna, anakumana ndi mkango ndipo unayamba kubangula. 6 Ndiyeno mzimu wa Yehova unamupatsa mphamvu,+ moti anakhadzula mkangowo pakati ngati mmene munthu angakhadzulire kamwana ka mbuzi ndi manja. Koma sanauze bambo kapena mayi ake zimene anachitazi.

  • Oweruza 14:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno mzimu wa Yehova unamupatsa mphamvu.+ Choncho anapita ku Asikeloni+ nʼkukapha amuna 30 akumeneko, ndipo anatenga zovala zawo nʼkuzipereka kwa anthu amene anamasulira mwambi aja.+ Iye anali wokwiya kwambiri pamene ankabwerera kunyumba ya bambo ake.

  • Oweruza 15:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atafika naye ku Lehi, Afilisiti nʼkumuona, anafuula chifukwa chosangalala. Ndiyeno mzimu wa Yehova unamupatsa mphamvu,+ ndipo zingwe zimene anamʼmanga nazo manja zija zinadukaduka ngati ulusi wowauka ndi moto nʼkugwa pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena