-
1 Samueli 3:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Samueli anagonabe mpaka mʼmawa. Atadzuka anatsegula zitseko za nyumba ya Yehova, koma ankaopa kuuza Eli za masomphenya amene anaona.
-