Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 2:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako mfumu inaitanitsa Simeyi+ nʼkumuuza kuti: “Umange nyumba yako ku Yerusalemu ndipo uzikhala kumeneko. Usadzachokeko nʼkupita kwina kulikonse. 37 Tsiku limene udzachoke nʼkudutsa chigwa cha Kidironi,+ udziwiretu kuti udzafa. Mlandu wa magazi ako udzakhala pamutu pako.”

  • 2 Mbiri 30:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako iwo anakachotsa maguwa ansembe amene anali mu Yerusalemu.+ Anachotsanso maguwa onse a nsembe zofukiza+ nʼkukawataya kuchigwa cha Kidironi.

  • Yohane 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Atamaliza kunena zinthu zimenezi, Yesu anatuluka limodzi ndi ophunzira ake nʼkuwoloka chigwa cha Kidironi+ kupita kumene kunali munda. Iye ndi ophunzira akewo analowa mʼmundamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena