-
Yona 1:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Koma Yona ananyamuka nʼkulowera ku Tarisi, kuthawa Yehova. Atafika ku Yopa anapeza chombo chopita ku Tarisi. Iye analipira ndalama za ulendowo pothawa Yehova nʼkukwera chombocho kuti apite ku Tarisi limodzi ndi anthu amene anali mmenemo.
-