Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 24:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ngakhale kuti asilikali a Siriya amene anabwera anali ochepa, Yehova anapereka mʼmanja mwawo gulu lalikulu kwambiri la asilikali+ chifukwa iwo anasiya Yehova Mulungu wa makolo awo. Choncho Asiriyawo anapereka chiweruzo kwa Yehoasi. 25 Asilikaliwo atachoka (nʼkumusiya atavulala kwambiri), atumiki ake anamʼkonzera chiwembu chifukwa anapha ana* a wansembe Yehoyada.+ Iwo anamuphera pabedi lake.+ Kenako anamuika mʼmanda mu Mzinda wa Davide+ koma sanamuike mʼmanda a mafumu.+

  • 2 Mbiri 28:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kenako Ahazi, mofanana ndi makolo ake, anamwalira ndipo anaikidwa mʼmanda mumzinda wa Yerusalemu. Iye sanaikidwe mʼmanda a mafumu a Isiraeli.+ Ndiyeno Hezekiya mwana wake anakhala mfumu mʼmalo mwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena