Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 15:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Kumapeto kwa zaka 7 zilizonse muzimasula anthu amene anakongola zinthu zanu.+ 2 Muzichita izi pomasula anthu angongolewo: Munthu aliyense azimasula mnzake amene ali ndi ngongole yake. Asamakakamize mnzake kapena mʼbale wake kuti abweze ngongoleyo, chifukwa chilengezo choti anthu angongole amasuke chaperekedwa potsatira lamulo la Yehova.+ 3 Mlendo mungathe kumukakamiza kuti abweze ngongole,+ koma ngati mʼbale wanu wakongola chinthu chanu chilichonse, musamukakamize kuti achibweze.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena