Nehemiya 2:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Ndiyeno Sanibalati wa ku Beti-horoni, Tobia+ mtumiki wa Chiamoni+ ndi Gesemu Mluya+ atamva zimenezi anayamba kutiseka ndi kutinyoza.+ Iwo anati: “Nʼchiyani chimene mukuchitachi? Kodi mukugalukira mfumu?”+ Nehemiya 4:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Tobia+ Muamoni,+ yemwe anaima pambali pake anati: “Ngakhaletu nkhandwe itakwera pampanda wamiyala umene akumangawo ikhoza kuugwetsa.” Nehemiya 6:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Inu Mulungu wanga, kumbukirani Tobia+ ndi Sanibalati komanso zimene anachitazi. Mukumbukirenso Nowadiya mneneri wamkazi ndi aneneri onse amene ankafuna kundiopseza. Nehemiya 13:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kenako ndinafika ku Yerusalemu ndipo ndinaona zoipa zimene Eliyasibu+ anachita popatsa Tobia+ chipinda mʼbwalo la nyumba ya Mulungu woona.
19 Ndiyeno Sanibalati wa ku Beti-horoni, Tobia+ mtumiki wa Chiamoni+ ndi Gesemu Mluya+ atamva zimenezi anayamba kutiseka ndi kutinyoza.+ Iwo anati: “Nʼchiyani chimene mukuchitachi? Kodi mukugalukira mfumu?”+
3 Tobia+ Muamoni,+ yemwe anaima pambali pake anati: “Ngakhaletu nkhandwe itakwera pampanda wamiyala umene akumangawo ikhoza kuugwetsa.”
14 Inu Mulungu wanga, kumbukirani Tobia+ ndi Sanibalati komanso zimene anachitazi. Mukumbukirenso Nowadiya mneneri wamkazi ndi aneneri onse amene ankafuna kundiopseza.
7 Kenako ndinafika ku Yerusalemu ndipo ndinaona zoipa zimene Eliyasibu+ anachita popatsa Tobia+ chipinda mʼbwalo la nyumba ya Mulungu woona.