Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Abulahamu anamwalira ali wokalamba, atakhala ndi moyo wabwino, wautali komanso atakhutira ndi moyo wake ndipo anaikidwa mʼmanda ngati mmene anachitira ndi makolo ake.*

  • 2 Mafumu 22:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Nʼchifukwa chake ndidzakuika mʼmanda a makolo ako ndipo udzaikidwa mʼmanda ako mwamtendere. Maso ako sadzaona tsoka lonse limene ndidzabweretse pamalo ano.’”’” Kenako iwo anakauza mfumuyo zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena