Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mawu apakamwa panga komanso zimene ndimaganizira mozama mumtima mwanga,

      Zizikusangalatsani, inu Yehova,+ Thanthwe langa+ ndiponso Wondiwombola.+

  • Yesaya 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mʼmalo mopeza mtendere ndinali ndi chisoni chachikulu.

      Koma chifukwa chakuti mumandikonda kwambiri,

      Munanditeteza kuti ndisapite kudzenje lachiwonongeko.+

      Machimo anga onse mwawaponyera kumbuyo kwanu.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena