Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pa tsikuli, mmodzi wa atumiki a Sauli anali kumeneko chifukwa anali atamusunga pamaso pa Yehova. Dzina lake anali Doegi+ ndipo anali wa ku Edomu.+ Iye anali mkulu wa abusa a Sauli.

  • Salimo 94:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, kodi anthu oipa adzapitiriza kusangalala mpaka liti?

      Adzapitiriza kukondwera mpaka liti?+

       4 Zolankhula zawo zimasonyeza kuti ndi opusa komanso onyada.

      Anthu onse ochita zoipa amalankhula modzitama.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena