Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 62:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndithudi, ndikuyembekezera* Mulungu modekha.

      Chipulumutso changa chimachokera kwa iye.+

       2 Iye ndi thanthwe langa komanso ndi amene amandipulumutsa, malo anga othawirako otetezeka.*+

      Sindidzagwedezeka kwambiri.+

  • Salimo 71:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa chiyembekezo changa ndi inu Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.

      Ndakhala ndikudalira inu kuyambira ndili mnyamata.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena