Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 44:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Dzukani. Nʼchifukwa chiyani mukugonabe, inu Yehova?+

      Dzukani. Musatitaye kwamuyaya.+

  • Yesaya 64:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Poona zinthu zonsezi, kodi mupitiriza kumangokhala osachitapo kanthu, inu Yehova?

      Kodi mungokhala chete nʼkumaonerera ife tikusautsidwa koopsa?+

  • Maliro 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye wathetsa mphamvu zonse za* Isiraeli atakwiya kwambiri.

      Adani athu atatiukira, iye sanatithandize,+

      Ndipo mkwiyo wakewo unapitiriza kuyakira Yakobo ngati moto umene wawononga chilichonse chimene chili pafupi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena